Nkhani
Maneb ikhutila ndi mayeso a sitandade 8
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Staff Writer
Bungwe loyendetsa mayeso la Malawi National Examinations Board (Maneb) lati lakhutira ndi mmene mayeso a Sitandade 8 ayambira.
Konvenshoni ya MCP yalephereka
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Kondwani Kamiyala
Chipani cha Malawi Congress Party (MCP) chati msonkhano wake waukulu wa konvenshoni umene umayenera kukhalapo pakati pa lero ndi Lolemba wamwa madzi.
Anthu a ku Likoma alirira Ilala
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Staff Writer
Anthu okhala pazilumba za Likoma ndi Chizumulu ati akulira ndipo moyo ukutentha chifukwa cha kusiya kuyenda kwa sitima ya Ilala.
Zipolowe zikuphulika
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Steven Pembamoyo
Pamene tikuyandikira chaka cha 2014 pomwe Amalawi akuyembekeza chisankho cha magawo atatu chosankha Pulezidenti, aphungu a Kunyumba
Bajeti iganizire mavuto a anthu
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Steven Pembamoyo
Ndondomeko ya chuma ndiyo chiyembekezo chachikulu tsopano chomwe chingachepetse mavuto omwe anthu akukumana nawo kaamba ka kukwera mitengo ya zinthu m’dziko muno.
Wailesi ya Dzimwe ikusowa thandizo ku Mangochi
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by RACHAEL KACHALI
Nyumba youlutsira mawu ya Dzimwe Community Radio ku MonkeyBay m’boma la Mangochi yapempha thandizo lomangira ofesi komanso kugula zida zoulutsira mawu kuchokera kwa akufuna kwabwino.
‘Boma likweza malipiro’
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Steven Pembamoyo
Ogwira ntchito angasimbe lokoma ngati ganizo la unduna wa zantchito lokweza malipiro otsikitsitsa amene amalandira lingafitsidwe.
Konvenshoni ya MCP pa 28 April
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Steven Pembamoyo
Pamene chipani cha Malawi Congress Party (MCP) chatsimikiza kuti msonkhano wake waukulu wokasankha atsogoleri udzachitika pa 28 ndi 29 Epulo, katswiri wa zandale Dr Mustapha Hussein wadzudzula mchitidwe wosintha malamulo oyendetsera chipani n’cholinga chopatsa mpata anthu omwe sakuloledwa kupikisana nawo pamaudindo kuti atero.
Apolisi anjatidwa pokhudzidwa ndi ophedwa pa zionetsero
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Staff Writer
Apolisi asanu ndi anayi adatengedwa m’sabatayi powaganizira kuti akudziwapo kanthu pa za ena amene adaphedwa pazionetsero za pa 20 Julaye 2012.
Olephera asatuluke DPP—Mutharika
- Category: Nkhani
- Published Date
- Written by Emmanuel Muwamba
EMMANUEL MUWAMBAYemwe anali mtsogoleri wogwirizira mpando wa pulezidenti wa chipani cha DPP, Peter Mutharika, Lachinayi adalangiza omwe amapikisana nawo pofuna mipando yosiyanasiyana kuti akalephera si bwino kuchoka m’chipanicho.
Tamvani
