Thursday, January 28, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

40 awaganizira kugwa m’ndenge yamatsenga

by Gladson M'bumpha
20/08/2016
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Anthu 40 m’boma la Ntchisi akuwaganizira kuti adagwa m’ndege yamatsenga yomwe anthuwo adakwera akuchokera kotamba.

Nkhaniyi idadzidzimutsa anthu ambiri okhala m’mudzi mwa Chikuta m’dera la mfumu yaikulu Chilooko m’bomali Lachitatu pa 17 August pomwe chinthu china chachilendo, chomwe akuchiganizira kuti ndi ndege ya ufiti, chidagwa m’mudzimo.

RelatedHeadlines

Zisangalalo zafika, samalani

Mademo ayambika

Makhansala aderera alawansi

Phiri: Nayi ndenge ya matsenga
Phiri: Nayi ndenge ya matsenga

Malingana ndi sing’anga Pilirani Phiri wa m’mudzi mwa Ziwanda m’dera la

tidaitenga pamodzi ndi amfumu a m’mudzimo n’kupita nayo kupolisi ya Kamsonga komwe ndipo apolisi adatiuza kuti, ngati sing’anga, ine ndi amene ndingathe kuononga ndegeyo ndipodi ndidakaonongadi poitentha,’’ adatero Phiri.

Titamfunsa kuti adadziwa bwanji kuti m’ndegemo mudali anthu 40, Phiri adati adaunika ndi galasi lake lomwe amaonera zamatsenga ndipo onse amene adali mmenemo akuwadziwa ndipo achikhala kuti boma limavomereza bwenzi akuluakuluwo atawatumizira “nuclear” kuti akhaule chifukwa akumaphunzitsa ana ufiti “koma ndikatero ndiye kuti ndiika miyoyo ya makolo a anawo pachiopsezo chifukwa abale a mfitizo akhoza kukawachita chipongwe”.

“Ngakhale ena akuti ufiti kulibe, kunja kuno kukuchitika zoopsa ndipo zimatengera sing’anga amene adazama kuti adziwe zomwe zikuchitika,” adatero sing’angayo.

Mkulu wa polisi pa Kamsonga Police Unit, Inspector Kennedy Kwalira, adatsimikiza za nkhaniyi.

Iye adati nkhaniyi adailandiladi ndipo ngati apolisi sakanatha kutengapo gawo pankhaniyo koma kuuza sing’angayo kuti ndi amene adakatha kuononga ndegeyo chifukwa malamulo a dziko lino savomereza kuti kunja kuno kuli ufiti.

Previous Post

Could the elderly be solution to albino myths?

Next Post

Development should not be about laying foundation stones!

Related Posts

Malango: We are addressing challenges
Nkhani

Zisangalalo zafika, samalani

December 11, 2020
Pazionetsero za HRDC, chimbaula cha polisi chidaotchedwa
Nkhani

Mademo ayambika

December 11, 2020
Councillors in Mzuzu Nov 2020 | The Nation Online
Nkhani

Makhansala aderera alawansi

December 5, 2020
Next Post

Development should not be about laying foundation stones!

Trending Stories

  • Walking in her late mother’s shadows: Miracle

    New mashup draws mixed reactions

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Donors up game in Covid-19 fight

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • SA returnees in forced quarantine

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Budget off rails

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Spread hope not fear

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Opinions and Columns

My Turn

When schools become inaccessible, a glimmer of hope in a coding boot-camp

January 27, 2021
My Turn

Behaviour change key in Covid-19 fight

January 25, 2021
Emily Mkamanga

Citizens power brings change

January 24, 2021
Search Within

The rural farmer needs to take centre stage

January 24, 2021
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.