Wednesday, May 25, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

‘Aphungu apite m’midzi’

by Johnny Kasalika
28/04/2012
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Pomwe sipikala wa nyumba ya malamulo, Henry Chimunthu Banda walengeza Lachitatu m’sabatayi kuti aphungu ayamba kukumana pa 18 Meyi, T/A Mwakaboko ya m’boma la Karonga yati aphunguwa akuyenera apite kumudzi kukamva zomwe anthu awo akufuna kuti akakambirane.

Mfumuyi yati aphunguwa amangonama kuti zomwe akukambiranazo zikuchoka kwa anthu omwe adawasankha chikhalirecho samapitako.

Mwakaboko wati aphungu akumakhala m’tauni zomwe zikulepheretsa kuti mbalizi zizikambirana zosowekera za dera lawo.

Mfumuyi yati ikhala yokondwa kuti pakhale yankho la mavuto a kusowa kwa mafuta agalimoto.

Mwakaboko watinso njira yosankhira ophunzira opita kusukulu ya ukachenjede ikuyeneranso kukambidwa.

“Mukumbuka bwino kuti kuno takhala tikudandaula ndi ndondomokoyi ndiye ndibwino aphunguwo akakambirane zimenezi,” adatero Mwakaboko.

William Joseph wa m’mudzi mwa Goveya kwa T/A Makwangwala ku Ntcheu wati pa 18 pasadafike aphunguwa apite kumudzi kukafunsa osati kumangowaimbira lamya pazomwe akakambirane.

Mlimi wa chimangayu wati ndibwinonso kuti aphunguwa akakambirane

zochotsa ndondomeko yosadalira chithandizo chakunja ya Zero-deficit.

Iye wati anthu avutika kwambiri maka pokwera misonkho kwa zinthu chifukwa cha ndondomekoyo.

Previous Post

Ma MP olowa PP akonzekere nkhondo

Next Post

DPP can’t lead opposition—JZU

Related Posts

Nkhani

Agwidwa ndi yunifomu za polisi

May 22, 2022
Nkhani

Dollar yasowa

May 21, 2022
Foni kundende monga ya Zomba n’zoletsedwa
Nkhani

Apezeka ndi foni m’mimba

May 15, 2022
Next Post
The Nation Online DPP can’t lead opposition—JZU

DPP can’t lead opposition—JZU

Opinions and Columns

People’s Tribunal

What was that press briefing all about?

May 22, 2022
Big Man Wamkulu

Wife, in-law plotting my downfall

May 22, 2022
My Thought

Tonse Alliance died on arrival

May 22, 2022
Layman's Reflection

New IMF programme pivotal moment for Tonse Alliance

May 21, 2022

Trending Stories

  • Kalindo: I am hearing it from you

    Kalindo earmarked for diplomatic post

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Musician Martse in hospital after fire accident

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Cooking oil project impresses Chilima

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Musicians, fans mourn Martse

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Witness U-turns in Batatawala, 3 others case

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.