Wednesday, March 3, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Akufuna boma likweze malipiro

by Bobby Kabango
04/05/2018
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Bungwe loona za ufulu wa anthu ogwira ntchito la Malawi Congress of Trade Union (MCTU) lapempha boma kuti likweze mlingo wa ndalama zotsikitsitsa zomwe munthu angalandire, komanso kuti anthu amene amalandira ndalama zochepera K50 000 pamwezi asamakhome  msonkho.

Polankhula pamwambo wokumbukira tsiku la ogwira ntchito Lolemba ku Lilongwe, mkulu wa bungwelo Luther Mambala adapempha boma kuti lionjezere ndalama za ogwira ntchito zotsikitsitsa zichoke pa K25 000 kufika pa K45 000. Ndipo adati okhoma msonkho azikhala olandira K50 000 kupita mtsogolo osati K25 000 monga zilili pano.

RelatedHeadlines

Mtsutso pa zoika a Covid-19

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

Sukulu zitsegulidwanso

Luther Mambala | The Nation Online
Mambala: Zinthu zakwera

Mambala adati akufunitsitsa boma litengere nkhaniyi ku Nyumba ya Malamulo kuti aphungu akaikaimbirane. Nyumba ya Malamulo imayembekezeka kutsegulidwa dzulo ndipo aphungu akambirana ndondomeko ya chuma.

“Chiyembekezo chathu n’choti nkhaniyi ifike kwa aphungu amene angatithandize,” adatero Mambala.

Bungweli lidapemphanso boma kuti lipeze njira zothetsera kuzimazima kwa magetsi zomwe ati zakhudza makampani kuti azipeza phindu lokwanira zomwe zikupangitsa kuti ena awachotse ntchito.

Mneneri wa boma Nicholas Dausi adalangiza bungwelo kuti lipereke madandaulo awo ku unduna wa zachuma omwe ungatengere nkhaniyi ku Nyumba ya Malamulo.

“Sindinganene zomwe boma lichite koma kungowalangiza kuti nkhaniyi aitengere ku unduna wa zachuma womwe ungatsatize bwino nkhaniyi,” adatero Dausi.

Previous Post

MBC flies three innovators to China

Next Post

Moto buuu! 2019 yafukiza zipani

Related Posts

covid death | The Nation Online
Nkhani

Mtsutso pa zoika a Covid-19

February 28, 2021
HRDC pursuing this matter further: Trapence
Nkhani

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

February 27, 2021
Teachers KK | The Nation Online
Nkhani

Sukulu zitsegulidwanso

February 27, 2021
Next Post
Kumsonkhano wa Aford ena adachita kugona komweko

Moto buuu! 2019 yafukiza zipani

Opinions and Columns

My Turn

Unmasking Covid-19 vaccine

March 3, 2021
My Turn

Tackling global slowdowns

March 1, 2021
People’s Tribunal

Burglary at the hill

February 28, 2021
Search Within

Perseverance landed, is alive and well

February 28, 2021

Trending Stories

  • Under probe: The Reserve Bank building in Mzuzu

    Exclusive: RBM’s Mzuzu branch payment mess exposed

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • K5bn Sunbird Waterfront hotel opens May

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Lhomwe chiefs divided on paramount chief

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Inside Chisale’s seized property

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Experts fault IFMIS roll-out delays

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.