Saturday, July 2, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Akufuna wogwirizira ufumu achoke, apepese

by Johnny Kasalika
18/08/2012
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Mafumu m’dziko muno agwirizana ndi ganizo la mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda kuti magulupu ndi nyakwawa asiye kulandirira ndalama kubanki.

Banda adalankhula izi sabata yatha pasukulu ya Nsumwa m’boma la Salima poyankha pempho la mfumu Ndindi kuti mafumu akuvutika pokalandirira ndalama kubanki.

Polandira Banda, Ndindi adati ndondomeko yomwe idayambitsidwa m’boma la chipani cha DPP kuti iwo adzikalandilira mswahala kubanki yazunza mafumuwa ponena kuti ndalamayo imathera ulendo.

Apa Banda adati nyakwawa ndi magulupu asamakalandirirenso ndalama kubanki ponena kuti ndondomeko yapoyamba ibwezeretsedwa.

Apa mafumuwa ati nkhaniyi iwathandiza chifukwa ndalamayo samaiwona ubwino wake malinga n’kuti komwe kuli mabanki ndi komwe amakhala ndi mtunda wautali.

Nyakwawa Kapoti ya kwa T/A Zilakoma m’boma la Nkhata Bay yati kuchokera m’mudzimo kukafika kuboma komwe kuli mabanki ndi mtunda omwe amalipira K2 000 kupita ndi kubwera.

Mfumuyi yauza Tamvani kuti penanso akapita ndalamazo amakapeza zisadalowe.

“Ndimalandira K2 500 ndipo ndimaononga K2 000 kusonyeza kuti malipiro anga ndi K500. Apa tiyamike kuti tizilandira kumudzi kuno,” idatero mfumuyo.

Gulupu Chisinkha ya m’boma la Mulanje kwa T/A Mabuka yati mfundo ya boma ili bwino bolani ndalamazo adziwapatsadi.

“Ndondomeko yapoyambayonso idali ndi mavuto ake pomwe pena malipiro sitimalandira. Ganizoli n’labwino bola tizilandira,” adatero Chisinkha.

Mtsogoleri wakale wa dziko lino, Bingu wa Mutharika ndiye adalamula kuti aliyense wogwira ntchito m’boma kuphatikiza mafumu adzikalandira malipiro awo kubanki.

Previous Post

The lost glory of Youth Week

Next Post

47 firms fight for subsidy contracts

Related Posts

Chilima: Change the mindset toward development
Nkhani

A Chilima abwera poyera

July 1, 2022
Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Katundu wa a Mtambo adali kuseri kwa ofesi za khonsolo
Nkhani

Agona ku maofesi a khonsolo ya Mzuzu

June 4, 2022
Next Post
The Nation Online 47 firms fight for subsidy contracts

47 firms fight for subsidy contracts

Opinions and Columns

My Diary

God-fearing nation, my foot!

July 2, 2022
Off the Shelf

APM digging a hole for DPP

July 2, 2022
Guest Spot

‘Fighting corruption is not the easiest task of any govt’

July 2, 2022
My Turn

Following spouse is no crime

July 1, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • Alliance partners talk

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • New VP houses draw criticism

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  •  Malawi credit Status at risk

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Britain squeezes Zuneth Sattar

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Chilima opens pandora’s box

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.