Tuesday, July 5, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Anthu 50 000 akutenga HIV chaka chilichonse

by Staff Writer
25/05/2012
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Pamene nkhondo yolimbana ndi matenda a Edzi ikupitirira, zadziwika kuti chaka chilichonse anthu 50 000 akutenga kachirombo ka HIV kamene kamayambitsa matendawa.

Polankhula pamwambo woganizira anthu amene adataya miyoyo yawo kaamba ka nthendayi komanso amene ali ndi kachirombo koyambitsa nthendayi, wachiwiri kwa pulezidenti wa dziko lino Khumbo Kachali adati aliyense ayenera kutengapo gawo kuti chiwerengerochi chitsike.

“Ndi udindo wa tonse kulimbana ndi matenda a Edzi ndipo tonse tiyenera kuyezetsa,” adatero Kachali, yemwenso ndi nduna ya zaumoyo.

Mkulu wa bungwe la UNAIDS ku Malawi Patrick Brenny adati Malawi ikuchita bwino pankhondo yolimbana ndi matendawa.

“Malawi akuchita bwino makamaka makamaka pankhani ya kadyedwe, kuchepetsa kupatsirana kwa nthendayi pakati pa mayi ndi mwana komanso ma ARV,” adatero iye.

Koma Brenny adati n’kofunika kuti Amalawi agwirane manja ndipo asatope popewa matendawa.

Pamwambowo, wogwira ntchito kuwailesi Wesely Kumwenda adati atolankhani amene adapezeka ndi HIV ayenera kubwera poyera. Iye adati ngakhale adamupeza ndi HIV zaka 10 zapitazo, alibe nkhawa, ndipo wabereka ana awiri pakatipa.

Previous Post

Financial advisor for others—what about yourself?

Next Post

Beckoned by destiny

Related Posts

Chilima: Change the mindset toward development
Nkhani

A Chilima abwera poyera

July 1, 2022
Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Katundu wa a Mtambo adali kuseri kwa ofesi za khonsolo
Nkhani

Agona ku maofesi a khonsolo ya Mzuzu

June 4, 2022
Next Post

Beckoned by destiny

Opinions and Columns

My Turn

Child neglect and street robbery

July 4, 2022
Editor's Note

MPs’ houses to cost taxpayers K60bn

July 3, 2022
My Thought

Women underutilise digital platforms

July 3, 2022
Big Man Wamkulu

Her body count is too high, should I dump her?

July 3, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • APM, Ntaba risk Criminal charges

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Artists revel in presidential awards

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Dubai firm cries foul

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Bank questions import substitution rhetoric

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Her body count is too high, should I dump her?

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.