Friday, May 20, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Aphungu akana makondomu aulere

by Steven Pembamoyo
04/10/2020
in Nkhani
2 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Aphungu a Nyumba ya Malamulo Lachitatu adabweza mphatso ya makondomu 206 000 yomwe bungwe la Aids Health Foundation (AHF) lidapereka kunyumbayo.

Aphunguwo adakhumudwa ndi zomwe adanena wapampando wa komiti ya zaumoyo Maggie Chinsinga kuti aphungu, ogwira ntchito kunyumbayo komanso alendo amagwiritsa ntchito makondomu 10 000 pa mwezi.

Koma Lachitatu, aphungu a mbali zonse ziwiri ya boma ndi yotsutsa adanyangala ndi lipotilo lomwe adati ndi lochotsa ulemu komanso lonyazitsa ndipo adagwirizana zobweza mphatso yamakondomuyo.

Wachiwiri woyamba kwa sipikala wa nyumbayo Madalitso Kazombo sadapereke chigamulo chake pamtsutsowo, aphungu osiyanasiyana adapereka maganizo awo osonyeza kunyansidwa.

Pomaliza pa nkhaniyo, Kazombo adavomerezana ndi aphunguwo kuti mawu omwe adanenedwawo adachepsa ulemu wa aphungu ndipo adati mphato yamakondomuyo ibwezedwe komanso Chinsinga apepese.

Mkulu wa bungwe la AHF Triza Hara adati adapereka mphatso ya makondomuyo pofuna kuteteza aphungu, ogwira ntchito ku nyumbayo komanso alendo.

“Aliyense mwa iwo ayenera akhale ndi mpata umenewu odziteteza ku matenda,” adatero Hara.

Malingana ndi Chinsinga, mmbuyomo, nyumbayo imalandira makondomu kuchokera kuofesi ya zaumoyo m’boma la Lilongwe koma kenako idapanga ubale ndi bungwe la Partners in Hope.

Previous Post

Dorothy Sulani: Abandoned because of three children with disabilities

Next Post

Akumba manda m’khonde la nyumba

Related Posts

Foni kundende monga ya Zomba n’zoletsedwa
Nkhani

Apezeka ndi foni m’mimba

May 15, 2022
A Kamuzu adali katakwe pandale
Nkhani

‘Kamuzu adali chitsime chakuya’

May 14, 2022
Kodi chilango chonyonga chikhalepo, kapena ayi?
Nkhani

Amalawi akupereka maganizo pa zonyonga

May 14, 2022
Next Post

Akumba manda m’khonde la nyumba

Opinions and Columns

Business Unpacked

Fixing economy needs action, not rhetoric

May 19, 2022
Candid Talk

Know your place in his/her life

May 15, 2022
People’s Tribunal

Why can’t we start with implementing the reforms?

May 15, 2022
Big Man Wamkulu

My wife is a WhatsApp addict

May 15, 2022

Trending Stories

  • CAF accepts FAM’s request on Flames fixture shift

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Onesimus leaves Major One Records

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • MCTU pushes for 75% minimum wage hikeof

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Road traffic spot fines on way out

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Mayors may face ballots

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.