• Anatchezera

    Ndikufuna sukulu Zikomo Anatchereza, Ndine msungwana wa zaka 19. Sindidakwatiwepo, ngakhale sukulu ndidaisiyira Fomu 1 zaka zutatu zapitazo. Sukuluyo ndidasiya…

    Read More »
  • Anatchezera

    Za chikondi ndi chibwenzi Agogo, Kodi chibwenzi ndi chikondi ndi zosiyana bwanji? Mwina funso limeneli likhoza kuoneka ngati lopanda nzeru…

    Read More »
  • Anatchereza

    Wokondedwa Anatchereza, Zikomo chifukwa cha malangizo amene mukumapereka. Thandizeni. Ndili ndi mkazi yemwe ndakhala naye kwa nthawi ndithu. Iye adapezeka…

    Read More »
  • Anatchezera

    Ndimufunsirebe? Ndine mnyamata wa mu Lilongwe ndipo ndidagwa m’chikondi ndi msungwana wina. Ndakhala ndikuponya mawu kwa iye koma iyeyo amayankha…

    Read More »
  • Anatchezera

    Za Chikondi ndi chibwenzi Agogo, Kodi chibwenzi ndi chikondi ndi zosiyana bwanji? Mwina funso limeneli likhoza kuoneka ngati lopanda nzeru…

    Read More »
  • Anachezera

    Zidatheka! Zikomo Anatchereza, Ndafuna ndikuthokozeni kwambiri chifukwa cha malangizo anu. Pano tidamanga banja ndi mtsikana wa ku Machinga uja ndipo…

    Read More »
  • Anatchezera

    Chikondi amatero? Agogo, Ndine mtsikana wa zaka 20 ndipo ndili kukoleji. Ndili ndi chibwenzi chomwe tidagwirizana kuti tidzamange banja mtsogolo…

    Read More »
  • Anatchezera

    Akundimana Anatchereza, Ndakhala pabanja ndi mkazi wanga kuyambira mu 2011. Poyamba zonse zimayenda koma masiku ano ndikamufuna masiku ambiri amanena…

    Read More »
  • Anatchezera

    Ndazunguzika Agogo, Ndine mtsikana wa zaka 18 ndipo ndinazunguzika mutu chaka chatha pomwe ndinapezeka ndi kachilombo ka HIVkoma sindinagonepo ndi…

    Read More »
  • Anatchezera

    Akufuna mwana Zikomo Gogo, Banja ndi mwamuna wanga lidatha mu 2011. Ndidapeza mwamuna wina yemwe timamvana ndipo tidakayezetsa komwe adatipeza…

    Read More »
  • Anatchezera

    Anzanga sakundifunsira Ndine mtsikana wa zaka 20, vuto ndili nalo ndi loti sindikufunsiridwa ndi anyamata amsinkhu wanga koma okwatira okhaokha.…

    Read More »
  • Anatchezera

    Sakuthandiza Agogo, Ndine mtsikana wa zaka 21 ndipo ndili ndi mwana mmodzi. Amuna anga adandisiya ataona kuti ndili ndi pathupi…

    Read More »
  • ANATCHEZERA

    Wamkulu ndine Zikomo agogo, Ndili ndi chibwenzi koma timasiyana ndi chaka chimodzi, wamkulu ndineyo. Kodi tingathe kukwatirana? Iyeyu akufunitsitsa atandikwatira…

    Read More »
  • Anatchezera

    Sakufuna kukayezetsa Anatchereza, Ndakhala ndili pachibwenzi ndi mtsikana wina kwa chaka chimodzi ndipo timakondana kwambiri. Ndine Mkhristu ndipo ndikhulupirira kuti…

    Read More »
  • Anatchezera

    Ndisathandize mwana wanga? Anatchereza Ine ndi mkazi wanga tidalekana titakhala pabanja zaka ziwiri. Mkaziyu ndidakukwatira titachimwitsana pasukulu ine ndili Fomu…

    Read More »
  • Anatchezera

    Sagona m’nyumba Anatchereza, Ndili ndi zaka 20 ndipo amuna anga sagona m’nyumba ndiye chonde, ndithandizeni. Akuti ndikawauza ankhonswe banja langa…

    Read More »
  • Anatchezera

    Nditani Anatchereza? Agogo, Ndine mtsikana wa zaka 20 ndipo ndili ku koleji. Ndili ndi chibwenzi chomwe tidagwirizana kuti tidzamange banja…

    Read More »
  • Anatchezera

    Ndimamukonda Agogo, Ndinali pachibwenzi ndi mkazi wina ndipo zaka ziwiri zatha pomwe tinasiyana. Pano ali ndi mwana yemwe wabereka mwezi…

    Read More »
  • Anatchezera: Akukana kunditsata

    Agogo, Ndine mnyamata wa zaka 20 ndipo ndili pachibwenzi ndi mtsikana wa zaka 22 ndipo timakondana kwambiri koma vuto ndi…

    Read More »
  • anatchezera

    Amandimenya Zikomo gogo, Ndine mtsikana wa zaka 20 ndipo ndili pachibwenzi ndi mwamuna wa zaka 25. Tili ndi mwana mmodzi…

    Read More »
Back to top button