-
Chichewa
Akhazikitsa kamtengo pachipatala cha nkhalamba
Malingana ndi kuchuluka kwa anthu achikulire amene amabwera pachipatala cha anthu okalamba cha Kalibu Elderly Clinic ku Lirangwe m’boma la…
Read More » -
Chichewa
‘Pewani chukwu Ku mtedza’
Chukwu kapena aflatoxin m’Chingerezi ndi liwu lomwe silichoka pakamwa ku ulimi wa mtedza m’dziko muno chifukwa ndi chipsinjo chachikulu ku…
Read More » -
National News
Minister vows to punish errant contractors
Minister of Gender, Children, Disability and Social Welfare Mary Navicha has warned that her ministry will punish contractors that construct…
Read More » -
National News
Crop diversification could end hunger—Minister
Minister of Agriculture, Irrigation and Water Development Kondwani Nankhumwa has asked farmers in the country to diversify their farming to…
Read More » -
Chichewa
Tetezani ana ku BP
Chimodzimodzi akulu, ana nawo amakhala pachiopsezo cha matenda othamanga magazi choncho makolo akuyenera kuwateteza, watero mkulu wa pa chipatala cha…
Read More » -
Chichewa
Samalani ndi chitopa
Kuchokera ku phindu la ulimi wothirira, Catherine Bamusi wa m’boma la Blantyre adaganiza zogulako nkhuku zachikuda kuti zizimupatsa manyowa, ndiwo…
Read More » -
Chichewa
Akupha makwacha ndi nkhumba
Pamene alimi ena akugulitsa ziweto zawo kwa mavenda motsika mtengo, Chawezi Nyirenda yemwe ndi mlimi wa nkhumba ku Lilongwe akupha…
Read More » -
Chichewa
Muli mphamvu mu ukhondo
Bungwe la Water for People Malawi (WPM) lomwe cholinga chake n’kuonetsetsa kuti anthu m’dziko muno azimwa madzi aukhondo, komanso kukhala…
Read More » -
Chichewa
Kupewa chigodola cha nkhumba ndikotheka
M’mwezi wa February chaka chino mlimi wina wa nkhumba m’boma la Lilongwe, Jeofrey Kaiyatsa, adaona ngati malodza nkhumba zake zonse…
Read More » -
Chichewa
Ulimi wa njuchi ndi ofesi yonona
Kodi ulimi wa njuchi mudayamba liti? Ulimiwu ndidayamba mu 2017. Nanga chidakukopani n’chiyani? Nditalingalira mozama ndidaona kuti ulimi wa njuchi…
Read More » -
Chichewa
Sungani mbatata m’munda, M’nkhuti kuti isaonongeke
Alfred Mumba wa m’boma la Dowa amalima mbatata pa malo okwana maekala 5. Iye amapeza matumba osachepera 250 a mbatata…
Read More » -
National News
Project to improve hygiene, increase access to water in CZ
Water for People Malawi (WPM) and Chirazulu District Council have signed a three-year memorandum of understanding (MoU) that will see…
Read More » -
Chichewa
Osaiwala kuteteza mtedza ku chuku
Pamene mbewu ya mtedza yacha, katswiri wa mbewu za mtunduwu kwa Bvumbwe Richard Andasiki akuti alimi ateteze mbewuyi ku chuku…
Read More » -
Chichewa
Mafizo amathandiza anthu achikulire
Woona za mafizo pa chipatala cha anthu achikulire cha Kalibu ku Lilangwe m’boma la Blantyre Veronica Mughogho akuti mafizo ndiothandza…
Read More » -
Chichewa
Zinthu zitatu mu nkhuku imodzi ya Mikolongwe
Katswiri wa ulimi wa ziweto wa ku Lilongwe University of Agriculture and Natural Resources (Luanar) Timothy Gondwe wati kukhala ndi…
Read More » -
Chichewa
Tigwirane manja pothana ndi chisaka cha Nthochi
Mkulu woona za mbewu za m’gulu la zipatso ku dipatimenti ya za kafukufukuku mu unduna wa zamalimidwe Felix Chipojola akuti…
Read More » -
Chichewa
Akangalika ndi ulimi wa mthirira
Mlimi wochenjera monga NELLIE NYONI wa m’boma la Balaka amayambiratu ulimi wa m’chilimwe mvula ikamapita kumapeto kuti asavutike kwambiri ndikuthirira.…
Read More » -
Chichewa
Gwiritsani bwino ntchito chinyezi kuti mupindule
Potsatira mvula yochuluka yomwe yagwa m’chakachi, akatswiri a za kafukufuku wa ulimi wa mthirira akuti alimi a m’zigwa za dziko…
Read More » -
Chichewa
Tikolole motani chimanga?
Alimi m’madera a dziko lino amakolola chimanga mosiyanasiyana malingana ndi kuzolowera kwawo koma mphunzitsi wa kunthambi ya za maphunziro a…
Read More » -
Chichewa
Chenjerani pokolola
Mbewu ya chimanga nayo imafuna kuyichengetera nthawi yokolola kuti zokolola zikhale zochuluka ndi zopatsa kaso. Wachiwiri kwa mkulu woona za…
Read More »