Sunday, February 28, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Boma lititeteze, atero achitetezo

by Bobby Kabango
11/10/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

 

Anthu okhwimitsa chitetezo m’mudzi mwa Ntenje, m’dera la T/A Machinjiri m’boma la Blantyre, apempha boma kuti liwateteze ndi kuwasamala pamene akusaka malo obisala.

RelatedHeadlines

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

Sukulu zitsegulidwanso

Ayamikira boma pa ganizo lotsegulanso sukulu

Iwo ati pantchito yawo monga odzipereka, samalandira kalikonse koma pofuna kuteteza mudzi wawo, kwapezeka kuti nyumba zawo zatenthedwa, katundu waonongedwa. Miyoyo yawo ili pachiswe; iwo ndi mabanja awo akusowa pokhala; ndipo akubisala m’tchire.

crime e1440865089120 | The Nation OnlinePolice_chimbaula

Kumayambiriro a mwezi uno anthu okwiya a m’mudziwo adabutsa nyumba zawo, kuwakumbitsa manda komanso kuwamenya powaganizira kuti adapha munthu.

Monga akufotokozera mmodzi mwa achitetezowo, Davie Story, iwo ankateteza Nyadani Dankeni kuti asachitidwe chipongwe ndi anthu okwiyawo amene ankamumenya chifukwa chomuganizira kuti adaba thumba la chimanga.

Iye adati anthuwo adayatsa nyumba zawo ndipo palibe chomwe adapulumutsapo. Adawakumbitsa manda komanso kuwatibula kodetsa nkhawa. Achitetezo onsewo athawamo m’mudzimo ndipo akubisala m’tchire.

Mkulu wa achitetezowo, Damiano Dindi, adati iye adawathawira ku Nsanje.

“Palibe chomwe ndapulumutsa. Chonde, tikupempha boma kuti litithandize chifukwa tazingwa, tilibe pogwira komanso kolowera. Atipezere pokhala komanso atipatse mpamba woti tiyambire moyo wina,” adatero Dindi.

Previous Post

Dumped to die! Boy shot by cops claims

Next Post

Kwaterera kwa ntenje

Related Posts

HRDC pursuing this matter further: Trapence
Nkhani

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

February 27, 2021
Teachers KK | The Nation Online
Nkhani

Sukulu zitsegulidwanso

February 27, 2021
Flashback: Learners observing some of the Covid-19 protocols
Nkhani

Ayamikira boma pa ganizo lotsegulanso sukulu

February 19, 2021
Next Post
Akulephera kukhala chifukwa chovulazidwa m’matako: Story

Kwaterera kwa ntenje

Opinions and Columns

My Diary

Light that came with Covid-19

February 27, 2021
Guest Spot

Resurgence of albino killings deplorable

February 27, 2021
Back Bencher

Is violence a boomerang effect in DPP?

February 27, 2021
Off the Shelf

Sacrificial lambs of a dysfunctional system

February 27, 2021

Trending Stories

  • Court has declared Escom a private firm

    Court declares Escom private company

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • K1.7bn Chisale assets seized

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Inside Chisale’s seized property

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • What the hell is APM doing with BJ?

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • HRDC alleges threats, intimidation from investor

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.