Sunday, March 7, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Chilima akhazikitsa UTM ku Blantyre

by Nation Online
27/07/2018
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Saulos Chilima, mawa akhazikitsa gulu la United Transformation Movement (UTM) ku Njamba mu mzinda wa Blantyre.

Polankhula ndi Tamvani, mneneri wa gululi, Joseph Chidanti Malunga, adati chilichonse chokonzekera kukhazikitsidwaku chili mchimake.

RelatedHeadlines

Akana ndalama za Covid-19

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

VP security | The Nation Online
Chilima kukhazikitsa UTM pa bwalo la Masintha ku Lilongwe

“Tili ndi masomphenya a aakulu omwe amangiririka pa ndondomeko 12 zosinthira dziko lino. Anthu aku Lilongwe alawa kale zina mwa zinthu zomwe tikufuna kuchita,” adatero Malunga.

Msonkhanowu udayenera kukachitikira pa bwalo la sukulu ya Nyambadwe, koma Malunga adati asintha kaamba koti bwalolo ndi laling’ono.

Wapampando wa gululi, Noel Masangwi, adati ukatha msonkhano wa ku Blantyre, akakhazikitsanso gululo m’chigawo cha kumpoto.

Sabata yatha UTM idakhazikitsidwa pa bwalo la Masintha mu mzinda wa Lilongwe ndi chinantindi cha anthu chidafika pamwambowo.

Ena mwa anthu omwe adafika ndi Sipika wa Nyumba ya Malamulo, Richard Msowoya, akazi a atsogoleri akale a dziko lino, Callista Mutharika ndi Patricia Shanil Dzimbiri, phungu wa m’boma la Balaka, Lucius Banda, aphungu a DPP a m’boma la Mulanje, Bon Kalindo ndi Patricia Kaliati.

UTM idayambika Callista atapempha mtsogoleri wa dziko lino, Peter Mutharika, kuti apereke mwayi kwa Chilima kuti adzaimire DPP pa zisankho za chaka cha mawa.

Mutharika adakana pempholo zomwe zidachititsa kuti Chilima ndi anthu ena atuluke m’chipanicho n’kuyambitsa gulu la UTM.

Previous Post

Resources delay some PPP projects roll out

Next Post

UTM Ilembetsa ngatichipani—Malunga

Related Posts

covid relief | The Nation Online
Nkhani

Akana ndalama za Covid-19

March 6, 2021
Blantyre’s ‘best building’: St Michael and All Angels Church
Nkhani

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

March 6, 2021
People queue to buy maize at Admarc market
Nkhani

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

March 6, 2021
Next Post
Chilima gestures that those planning to rig the elections are in for trouble

UTM Ilembetsa ngatichipani—Malunga

Opinions and Columns

My Diary

Musowa voice missing yet needed

March 6, 2021
Off the Shelf

Off the Shelf 5 years on

March 6, 2021
Back Bencher

Let the teachers have their Covid-19 risk allowances

March 6, 2021
Guest Spot

Ensuring quality education for Malawian girls

March 6, 2021

Trending Stories

  • Lowe: We are trying to find potential markets

    Ministry plans to export 1m tonnes surplus maize

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • SKC ‘intervenes’ on youths’ demos

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Govt to finance 15 major projects

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Govt, TUM gloves off

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Let the teachers have their Covid-19 risk allowances

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.