Wednesday, May 25, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

‘Kudali ku Spar ya ku City Centre’

by Martha Chirambo
30/08/2020
in Chichewa
2 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Beatrice Mushani adakayamba ntchito ku Spar ya ku City Centre mu mzinda wa Lilongwe pa 1 October, 2018. Ndipo udali m’mawa wa tsikulo pomwe adakumana ndi Noel Kajani koyamba panja pa shopuyo, apa n’kuti akudikira kuti malowa atsegulidwe.

Panthawiyo n’kuti Kajani akugwira kale ntchito ku Spar konko.

Pang’onopang’ono awiriwo adayamba kucheza maka pomwe Mushani ankamufunsa Kujani kuti ntchito ya mu Spar imakhala bwanji.

“Pamene timadikira kuti titsegule shopu, ndi pomwe ndidamuonera Beatrice ndipo ndidali woyamba kuyankhula naye pomwe amadzayamba ntchito,” adalongosola Kajani.

Beatrice ndi Noel adakumana mushopu

Iye adati adakopeka ndi Mushani tsiku lomwelo ndipo patadutsa miyezi itatu adamufunsira.

Patadutsa chaka ndi miyezi 7 ali pa ubwenzi, awiriwo adakwatirana pamwambo wopambana omwe udachitikira ku Lewis Garden, mumzinda

wa Lilongwe pa 4 July 2020.

Iwo adati akakumana ndi mavuto amakhala pansi ndi kukambirana komanso amamupempha Mulungu kuti aziwathandizira.

Padakalipano Kajani akugwira ntchito kukampani ya Seed Co Malawi Limited pomwe Mushani amagwira ntchito ku Spar ya ku City Centre mumzinda wa Lilongwe.

Kajani amachokera m’mudzi mwa Gonthako, ka T/A Mabulabo, m’boma la Mzimba pomwe Mushani amachokera m’mudzi mwa Kadole, T/A Mwabulambia, m’boma la Chitipa. Koma iwowa akukhalira ku Area 12, mumzinda wa Lilongwe.

Previous Post

Hubby is too obsessed with me

Next Post

Agwiriridwa ali mtulo

Related Posts

Nkhani

Agwidwa ndi yunifomu za polisi

May 22, 2022
Nkhani

Dollar yasowa

May 21, 2022
Foni kundende monga ya Zomba n’zoletsedwa
Nkhani

Apezeka ndi foni m’mimba

May 15, 2022
Next Post

Agwiriridwa ali mtulo

Opinions and Columns

People’s Tribunal

What was that press briefing all about?

May 22, 2022
Big Man Wamkulu

Wife, in-law plotting my downfall

May 22, 2022
My Thought

Tonse Alliance died on arrival

May 22, 2022
Layman's Reflection

New IMF programme pivotal moment for Tonse Alliance

May 21, 2022

Trending Stories

  • Kalindo: I am hearing it from you

    Kalindo earmarked for diplomatic post

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Musician Martse in hospital after fire accident

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Cooking oil project impresses Chilima

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Musicians, fans mourn Martse

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Witness U-turns in Batatawala, 3 others case

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.