Sunday, February 28, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Mbali ina ya mnzinda wa Blantyre

by Chimwemwe Sefasi
15/11/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

local-shops

Kunena zoona, mzinda wa Blantyre ukusintha. Kuona momwe mzindawu akuukongoletsera, ukhoza kuyamika. Maluwa akubzalidwa ponseponse, misewu ndi misika ikukhala yosesedwa ngakhale mwina ndi mwina zinyalala zikutsalira. Posachedwa, taonanso akunena kuti nyumba zonse zosaoneka bwino zigumulidwe. Ndipo kunena za ku Limbe, msewu wa Highway nawo ukupatsa chikoka. Koma ukafika kumalo okwerera basi zosiyanasiyana kufupi ndi msika wa Limbe, kumene ambiri amati kokwerera galimoto za kwa Manje, umakhala ngati wafikanso tauni ina, osati Blantyre. Zisakasa izi ndi malo odyera. Ofika kumene m’tauni, amalonda, ogwira ntchito ena ngakhalenso ana asukulu akati akaone kadaunda madzi amalowa mmenemo. Kudya si kudya nanga?——chimwemwe sefasi

RelatedHeadlines

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

Sukulu zitsegulidwanso

Ayamikira boma pa ganizo lotsegulanso sukulu

Previous Post

Arrest Minister, health officers

Next Post

Osabweza ngongole ya Mardef ali m’madzi

Related Posts

HRDC pursuing this matter further: Trapence
Nkhani

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

February 27, 2021
Teachers KK | The Nation Online
Nkhani

Sukulu zitsegulidwanso

February 27, 2021
Flashback: Learners observing some of the Covid-19 protocols
Nkhani

Ayamikira boma pa ganizo lotsegulanso sukulu

February 19, 2021
Next Post
loan | The Nation Online

Osabweza ngongole ya Mardef ali m’madzi

Opinions and Columns

My Diary

Light that came with Covid-19

February 27, 2021
Guest Spot

Resurgence of albino killings deplorable

February 27, 2021
Back Bencher

Is violence a boomerang effect in DPP?

February 27, 2021
Off the Shelf

Sacrificial lambs of a dysfunctional system

February 27, 2021

Trending Stories

  • Court has declared Escom a private firm

    Court declares Escom private company

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • K1.7bn Chisale assets seized

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Inside Chisale’s seized property

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • What the hell is APM doing with BJ?

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • HRDC alleges threats, intimidation from investor

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.