Saturday, July 2, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Mikangano yatha

by Johnny Kasalika
07/04/2012
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Chisangalalo chadzanso kwa Achewa a m’boma la Mwanza pomwe T/A Kanduku wa m’bomalo walengeza Lolemba pa 26 Malitchi kuti madambwe onse omwe adawatseka atsekulidwenso.

Bwanamkubwa wa boma la Mwanza, Smart Gwedemula watsimikiza zakutsekulidwa kwa madambwewo.

Kanduku adatseka madambwewo ati pokhumudwa ndi zomwe Achewa amachita poumbudza amayi pomwe akuchokera kumadzi komanso kumumenya iyeyo popanda chifukwa.

Apa Kanduku adanyanyuka ndipo adatseka madambwewo chaka chatha.

Mafumu a Chichewa adauza Tamvani kuti zomwe akunena Kanduku kuti nyau zidamuumbudza ndi bodza koma kuti iye amakakamiza mafumu a Chichewo kuti alowe Chingoni popeza iye ndiwachingoni.

Mafumu angapo adaonetsa Tamvani mithini, mnyoni, zibonga ndi zishango zomwe mafumu Achichewawa amagwiritsa ntchito ati mokakamizidwa ndi Kanduku.

Mwezi wangothawu nduna ya maboma ang’ono, Henry Mussa idaitanitsa Kanduku.

Previous Post

Itching for an upset

Next Post

Eagles ready to spoil BB’s hopes

Related Posts

Chilima: Change the mindset toward development
Nkhani

A Chilima abwera poyera

July 1, 2022
Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Katundu wa a Mtambo adali kuseri kwa ofesi za khonsolo
Nkhani

Agona ku maofesi a khonsolo ya Mzuzu

June 4, 2022
Next Post

Eagles ready to spoil BB’s hopes

Opinions and Columns

Guest Spot

‘Fighting corruption is not the easiest task of any govt’

July 2, 2022
My Turn

Following spouse is no crime

July 1, 2022
Rise and Shine

Create your personal brand

June 30, 2022
Business Unpacked

We can do without some levies in fuel price

June 29, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • Entrance to one of the VP’s official residences in Blantyre: Mudi House

    New VP houses draw criticism

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  •  Malawi credit Status at risk

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Britain squeezes Zuneth Sattar

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • 4 DPP MPs disown Nankhumwa injunction

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Ex-MPC boss sues for unfair dismissal

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.