Sunday, February 28, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Msewu wa Rumphi-Nyika udzatheka?

by Nation Online
10/10/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Mkonzi,

Ndafuna ndipereke chidandaulo kuboma lathu kudzera m’nyuzi yathuyi komanso kwa phungu wa dera lathu la Rumphi West Hon Jacquilline Kouwenhoven kuti atiganizire za msewu wa Nyika womwe wakhala zaka zambiri osauganizira chonsecho ndi msewu wofunika kwambiri pachitukuko cha dziko lino, maka kumbali yokopa alendo.

RelatedHeadlines

Mtsutso pa zoika a Covid-19

Amwalira atathawa m’chipatala

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

Tsiku ndi tsiku alendo ochokera kumaiko akunja komanso ena a m’dziko mwathu mom’muno amadzera msewuwu kuchoka pa Rumphi boma kupita ku Nyika National Park kukacheza ndi kukaona zinyama. Kunena zoona, Nyika ndi malo okongola kwambiri ndipo amene adapitako amafananiza malowa ndi ku Mangalande. Koma ndikukaika ngati akabwerera kwawo amakhalanso ndi chilakolako choti adzabwererenso tsiku lina kumalowa chifukwa msewu wake ndi wosautsa kwambiri.

Msewu wopita kumalo okopa  alendowa ndi umenewu
Msewu wopita kumalo okopa
alendowa ndi umenewu

Nthawi yachilimwe ngati ino si mabamphu ndi fumbi lake kuchokera paboma kukafika ku Nyika moti alendo amakfika ali mbuu kutuwa ngati nyau komanso atatopa kotheratu. Nthawi yadzinja ndiyenso kumakhala ntchito chifukwa si matope ake moti ena amangobwerera paboma osakafika ku Nyikako.

Komanso msewu wa Nyikawu ndiye wachidule kwa anzathu omwe amakhala ku Nthalire ndi Wenya m’boma la Chitipa. Utakhala kuti waikidwa phula ndiye kuti nawonso awomboledwa kumbali ya maendedwe. Sakazunguliranso ku Karonga mpaka kukafika paboma la Chitipa kenaka n’kumalumikiza kukafika kwawo.

Ife alimi timavutika kwambiri kupita ndi katundu wathu kumisika chifukwa cha kuonongeka kwa msewuwu komanso timalipira ndalama zambiri tikakwera galimoto.

Chonde, nafe ndife Amalawi, tithandizeni.

G.V.H. Mpasula,

Rumphi

Previous Post

Who manned the gates?

Next Post

It is all your fault, Mr President

Related Posts

covid death | The Nation Online
Nkhani

Mtsutso pa zoika a Covid-19

February 28, 2021
death e1465557792659 | The Nation Online
Chichewa

Amwalira atathawa m’chipatala

February 28, 2021
HRDC pursuing this matter further: Trapence
Nkhani

‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’

February 27, 2021
Next Post

It is all your fault, Mr President

Opinions and Columns

People’s Tribunal

Burglary at the hill

February 28, 2021
Search Within

Perseverance landed, is alive and well

February 28, 2021
Emily Mkamanga

Tasting your own salt in politics

February 28, 2021
People’s Tribunal

When blood of citizens is on head of leaders

February 28, 2021

Trending Stories

  • chisale1 | The Nation Online

    Inside Chisale’s seized property

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • What the hell is APM doing with BJ?

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Admarc secures K430bn to revamp operations

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Grace Chinga makes posthumous return

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • K780M Dodma Covid-19 feast

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.