Saturday, March 6, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Ndege ya ufiti’ ikodwa ku Kasungu

by Dailes Banda
13/09/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Ngakhale malamulo a dziko lino amakana kumutchula munthu kuti ndi mfiti, Amalawi ambiri amakhulupirira kuti ufitu uliko.

Anthu a m’mudzi mwa Gundani m’boma la Kasungu adodoma ataona chinthu chooneka ngati ndege chomwe akuchiganizira kuti ndi ndege ya afiti chitagwa m’mudzimo.

RelatedHeadlines

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

Mtsutso pa zoika a Covid-19

The alleged witch craft plane that crashed

 

Msangulutso utafufuza chomwe chidachitikita, udapeza kuti ‘ndegeyo’ idagawa pakhomo pa Yusufu Abubaka Ali yemwe akukhulupilira kuti akola mfiti zomwe zakhala zikusautsa banja lawo.

“Anthu amenewa adalodza akazi anga koma ndi mmene agwidwiramu akazi anga akhala bwino,” adatero Ali.

Mkazi wa bamboyo Liness Kaulongo wakhala akudwala kwa nthawi yaitali ndipo kuchipatala cha boma ku Kasunguko adawauza akayesere zachikuda.

“Tidapita kwa asing’anga komwe adationetsa anthu anayi kuti ndi omwe akusautsa banja lathu. Sing’angayo adatipatsa mankhwala omwe adati tikaike panyumba yathu kuti ndidzakole mfiti zomwe zimanditambilazo,” adatero Ali.

Iye adati sanadabwe kwambiri mkazi wake akuuza kuti kunja kwa nyumba yawo kwagwa chinthu chooneka ngati ndege.

Kaulongo, adati adadabwa kuona chinthu chamaonekadwe ngati ndege chili panja panyumba yayo pomwe adatuluka usiku kukataya madzi.

Mneneri wapolisi m’boma la Kasungu Edwin Kaunda adatsimikiza kuti iwo akusungadi chinthu chomwe chikuganiziridwa kuti ndi ndege yaufiti.

Iye adati adapita pamalopo kukakhazikitsa bata chifukwa chinthucho chinkabweretsa mpungwepungwe pa malopo.

“Ife tidapita kukatenga chinthucho ndipo tili nacho kuno kupolisi,” adatero Kaunda.

Previous Post

Focus on healthy relationships

Next Post

Leaders use power to create self-importance

Related Posts

Blantyre’s ‘best building’: St Michael and All Angels Church
Nkhani

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

March 6, 2021
People queue to buy maize at Admarc market
Nkhani

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

March 6, 2021
covid death | The Nation Online
Nkhani

Mtsutso pa zoika a Covid-19

February 28, 2021
Next Post

Leaders use power to create self-importance

Opinions and Columns

My Diary

Musowa voice missing yet needed

March 6, 2021
Off the Shelf

Off the Shelf 5 years on

March 6, 2021
Back Bencher

Let the teachers have their Covid-19 risk allowances

March 6, 2021
Guest Spot

Ensuring quality education for Malawian girls

March 6, 2021

Trending Stories

  • Lowe: We are trying to find potential markets

    Ministry plans to export 1m tonnes surplus maize

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Govt to finance 15 major projects

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • SKC ‘intervenes’ on youths’ demos

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Exclusive: RBM’s Mzuzu branch payment mess exposed

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Covid-19 vaccine in today

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.