Monday, March 8, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Njovu ipha mlenje

by Malawi News Agency
08/01/2016
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Tsoka sasimba. Akanadziwa mlenje sakadapita kunkhalango ya Liwonde kukasaka nyama mozemba masiku apitawo.

Patrick Maya, wa zaka 52, ndipo amachokera m’mudzi mwa Chipala, Senior Chief Kawinga m’boma la Machinga, koma adasamukira m’mudzi mwa Wadi, Senior Chief Liwonde komwe amakhala ndi banja lake adafa njovu itamuponda.elephants

RelatedHeadlines

Akana ndalama za Covid-19

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

Malinga ndi mchimwene wa Maya, Maxwell Makina, iye adali ndi chizolowezi chosaka nyama mozemba pogwiritsanso ntchito agalu ake  m’nkhalango  ya Liwonde.

Makina adati pa tsiku la tsokali, Maya adalowa mkhalangoyi komwe sadabwererenso.

Iye adati ngakhale nkhani ya kusowa kwake idawapeza abalewa m’mudzi mwa Chipala  laMulungu lapitali, akukhulupilira kuti mlenjeyu adaphedwa pa Khirisimisi.

“Thupi lake lidapezeka Lamulungu pa 27 December, litaonongeka kale moti tidangosunga patchire pomwepo,” Makina adatero.

Wachiwiri kwa mneneri wapolisi kuchigawo cha ku m’mawa Otilia Kumanga watsimikiza za imfayi.

Previous Post

Si zonyengerera mu 2016—Mkulu wa polisi

Next Post

Aubameyang’s turn!

Related Posts

covid relief | The Nation Online
Nkhani

Akana ndalama za Covid-19

March 6, 2021
Blantyre’s ‘best building’: St Michael and All Angels Church
Nkhani

Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19

March 6, 2021
People queue to buy maize at Admarc market
Nkhani

Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside

March 6, 2021
Next Post
Aubameyang e1452258160147 | The Nation Online

Aubameyang’s turn!

Opinions and Columns

Search Within

Cut out the religious dogma from Covid-19 vaccines

March 7, 2021
Big Man Wamkulu

Won’t libido-boosting pills kill him?

March 7, 2021
Political Uncensored

Pulling rank…

March 7, 2021
People’s Tribunal

Ombudsman has challenged us all

March 7, 2021

Trending Stories

  • Protesting pay cut: Mathanga

    Court blocks RBM deputy governor salary cut

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • RBM sues Mulli, 4 others

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Police, DPP, ‘ignore’ court order

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Ministry plans to export 1m tonnes surplus maize

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Govt to finance 15 major projects

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.