Sunday, January 17, 2021
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Othawa nkhondo akutuwa ndi njala

by Bobby Kabango
19/06/2016
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

 

Kwathina kukampu ya anthu othawa nkhondo m’dziko la Mozambique amene akukhala ku Mwanza ndi Neno komwe anthuwa akutuwa ndi njala.

RelatedHeadlines

Amapita kukagula zomwera tiyi

Anatchezera

Odzipha akuchuluka

Ena atha sabata ziwiri tsopano popanda chakudya ndipo amene ali bwino ndi anthu amene adabwera ndi ndalama kuchokera m’dziko lawo.

Gulupu Ngwenyama wa m’boma la Mwanza wati anthuwa akusowa mtengo wogwira kupatula anthu amene adayenda ndi ndalama kuchokera m’dziko lawo.

Ndiwo ndi vuto lalikulu kwa othawa nkhondo
Ndiwo ndi vuto lalikulu kwa othawa nkhondo

“Amene adabwera ndi ndalama ndiwo sakulira kwambiri chifukwa akumagula zakudya, koma amene adangobwera opanda kanthu ndi amene akuvutika chifukwa akungodikira thandizo la mabungwe,” adatero.

Gulu la anthu lidayamba kukhamukira m’dziko muno kuchokera ku Mozambique komwe akugwebana pachiweniweni pakati pa otsutsa boma ndi aboma.

Kumenyanako, komwe kudayamba chaka cha

tha, kudafika poipitsitsa mu January pamene nzika zina za dzikolo zidayamba kuthawira m’dziko la Malawi.

Kampu ya Luwani ku Neno yomwe ikusunga anthu pafupifupi 1 400 njomwenso yakhudzidwa kwambiri ndi njalayi. Kampu ina ndi ya Kapise m’boma la Mwanza komwe kuli anthu pafupifupi 900.

Malinga ndi Ngwenyama, pali chiyembekezo kuti Lolemba likudzali bungwe la World Food Programme (WPF) ligawa chakudya kwa anthuwa.

Naye Senior Chief Saimoni wa m’boma la Neno wati mavuto a njala ndi osakambika chifukwa nthawi zonse kukumakhala mavuto.

Previous Post

‘Mudali m’galimoto ulendo ku Area 23’

Next Post

LDF defends maintaining Cashgate suspect

Related Posts

marriage | The Nation Online
Chichewa

Amapita kukagula zomwera tiyi

January 3, 2021
Chichewa

Anatchezera

January 3, 2021
An illustration of court proceedings
Chichewa

Odzipha akuchuluka

January 3, 2021
Next Post

LDF defends maintaining Cashgate suspect

Trending Stories

  • covid death | The Nation Online

    Tonse owes ‘ife tonse’ an apology

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Nocma in race against time

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Imbibers defy Covid-19 guidelines

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Locked with hubby’s brother

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Covid-19 mars cabinet review

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Opinions and Columns

Bottom Up

For 20 Pounds John Chilembwe was betrayed

January 16, 2021
My Diary

Tonse owes ‘ife tonse’ an apology

January 16, 2021
Off the Shelf

Accomplices in genocide

January 16, 2021
Back Bencher

On verge of collapse due to Covid-19

January 16, 2021
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2021 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Opinion
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

WhatsApp us

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.