Saturday, May 21, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Othawa nkhondo ku Mozambique asamukira ku Neno

by Patrick Lunda
07/05/2016
in Chichewa, Editors Pick
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Bungwe lothandiza anthu othawa kwawo pazifukwa zosiyanasiyana la UNCHR layamba kusamutsa anthu othawa nkhondo ku Mozambique kupita ku Luwani m’boma la Neno.

Anthuwa, omwe akuthawa  nkhondo yapachiweneweni, amafikira kumisasa yongoyembekezera m’maboma a ku Nsanje, Chikwawa, Mwanza komanso Neno omwe achita malire ndi dziko la Mozambique.

Bungwe la UNHCR lidayamba kusamutsa othawa nkhondowa sabata ziwiri zapitazi pamene anthu 81 adawapititsa ku Luwani m’boma la Neno kuchokera kumalo omwe amangodikirirapo ku Nsanje.

Ena mwa othawa nkhondo ku Mozambique ulendo  wa ku Luwani
Ena mwa othawa nkhondo ku Mozambique ulendo
wa ku Luwani

Mkulu wofalitsa nkhani kubungweli m’Malawi muno, Kelvin Shimoh, adati cholinga chawo ndi kuti othawa nkhondowa akhale malo amodzi komwe angakalandire thandizo lokwanira.

Iye adati pali pafupifupi anthu okwana 11 000 omwe athawa nkhondo kuchokera ku          Mozambique ndipo chiwerengerochi chikuyemebezeka kukwera kwambiri.

Ku Kapise m’boma la Chikwawa kuli anthu pafupifupi 10 000 ndipo akuyembekezeranso kusamutsidwa kupita ku Luwani komwe kuli malo abwino okhala, olandirira thandizo la mankhwala komanso  sukulu zoti ana omwe ndi ambiri azikaphunzirako.

Mkulu wina wa bungwe lomweli la UNHCR woona za chitetezo cha othawa kwawo, Elsie Bertha Mills-Tettey, wapemphanso dziko la Malawi ndi anthu onse kuti asawasale anthuwa powaganizira kuti ndi achiwembu.

“Kafukufuku wathu wapeza kuti anthu othawa nkhondowa ali pachipsinjo choopsa chifukwa ataya katundu wawo, abale awo ena aphedwa akuona, komanso ena mwa iwo apulumuka atazunzidwa,” adatero Mills-Tettey.

Iye wayamikiranso bungwe la Unicef pachithandizo chomwe likupereka kwa anthuwa nkhondowa, makamaka ana, pankhani zowambikitsa kuti apitirizebe maphunziro awo.

Previous Post

Man offers daughter for sale

Next Post

Reforms on microscope: Are they translating?

Related Posts

Nkhani

Dollar yasowa

May 21, 2022
Gwengwe: Closing the gap requires two things
Business News

World Bank sees widened fiscal deficit

May 21, 2022
A consumer loading prepaid electricity credit whose 
tariffs have been revised
Business News

Cama wants electricity tariffs reduced

May 21, 2022
Next Post
Asked to step down: Chilima

Reforms on microscope: Are they translating?

Opinions and Columns

Layman's Reflection

New IMF programme pivotal moment for Tonse Alliance

May 21, 2022
Family Table Talk

Historical lessons on the value of forgetting

May 21, 2022
My Diary

Politics of ‘kutola chikwama’

May 21, 2022
Bottom Up

Ukraine war: Sanctions backfire?

May 21, 2022

Trending Stories

  • Left economy in tatters: Muluzi

    Malawi’s public debt now at K5.8 tn

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • CAF accepts FAM’s request on Flames fixture shift

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Gaba comes up with two options

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Onesimus leaves Major One Records

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • UN bets K66bn on LMC’s plan

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.