Woimba abedwa mumzinda wa mzuzu
Anthu a m’dera la Mchenga-utuba mumzinda wa Mzuzu akukhala mwa mantha woimba wina wodziwika m’deralo atabedwa sabata yatha. Woimbayu Dickson...
Anthu a m’dera la Mchenga-utuba mumzinda wa Mzuzu akukhala mwa mantha woimba wina wodziwika m’deralo atabedwa sabata yatha. Woimbayu Dickson...
Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzidzi ya DoDMA yatolera K34.8 biliyoni ya ngozi zogwa mwadzidzidzi koma ndalamazo n’zochepa poyerekeza ndi...
Abambo ena 8 adabwitsa anthu ku Chibavi, mumzinda wa Mzuzu atapezeka ndi yunifomu zapolisi. Zovalazi ndi monga zigoba zovala panthawi...
Ntchito zambiri m’dziko muno zasokonekera kapena kuima kumene potsatira kusowa kwa ndalama zakunja zomwe zimagwiritsidwa ntchito poitanitsa katundu. Umboni wafika...
Nthambi ya zandende m’dziko muno yaimika kaye pantchito woyang’anira ndende Emmanuel Chiganda, yemwe mkaidi amene adapezeka ndi foni ziwiri m’mimba...
Pomwe Amalawi lero pa 14 May akukumbukira moyo ndi utsogoleri wa mtsogoleri woyamba a Hastings Kamuzu Banda, mizwanya pa mbiri...
Komiti yoona zamalamulo m’Nyumba ya Malamulo ili mkati motolera maganizo aanthu pa zachilango chonyonga opezeka wolakwa pa milandu ya kupha,...
Akadaulo a zandale ati mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera akuchedwa kuthothola mphamvu zina monga momwe adalonjezera. Bungwe la...
Kampani ya boma yogula ndi kugulitsa mbewu ya Admarc yati iyamba kugula chimanga mwezi wa mawa wa May ndipo yati...
Mtsogoleri wa Nyumba ya Malamulo a Richard Chimwendo Banda adatseka mkumano wa aphungu Lachitatu ndi langizo kwa otsutsa boma kuti...
Pamene mafuta ophikira akuyembekezeka kutsika mtengo kuyambira Lachisanu pa 1 April, komishoni yoona kuti pazikhala mpikisano wachilungamo pa malonda la...
Ali ndi zaka 17, mwanayu ankadwala matenda a muubongo omwe adabweretsanso mavuto olankhula pamoyo wake. Koma chimodzi chomwe mwanayu amakonda...
Womenyera ufulu pa nkhani zaumoyo, a George Jobe akumema makolo ndi onse omwe akusunga ana kuti aonetsetse kuti ana awo...
Akatswiri pa nkhani za ndale adandaula ndi kusasintha kwa zinthu m’dziko lino kwa zomwe zakhala zikuchitika kwa zaka zambiri. Mwa...
Nkhondo ndi anansi. Wodya naye mbale imodzi ndiye amakupereka kwa adani. Izi zapherezera kwa mwana wina wa zaka 11 yemwe...
Ndalama yatsopano ya K5 000 idayamba kugwira ntchito Lachinayi pa 24 February 2022 koma Amalawi ena akuda nayo nkhawa kuti...
Lucius Banda adaimba nyimbo yomwe imati: Takulira limodzi, kuyambira ubwana…. Kusiyana kwake n’koti anthu amaimbidwa m’nyimboyo mapeto sadakwatirane. Si zili...
Nduna ya zachuma a Sosten Gwengwe dzulo yalengeza bajeti ya 2022 mpaka 2023 yokwana K2.84 thriliyoni ndipo ati bajetiyo yapangidwa...
Ubwenzi wa James Mdala ndi Asiyatu James unayamba pa September 22 2020, mumzinda wa Lilongwe. Awiriwo anali atakumana miyezi iwiri...
Akuti tibwererane Anatchereza, Mmbuyomu ndidakwatiwa, koma banja lidatha ndipo ndidapeza mwamuna wina. Banja ndi mwamuna wachiwiri uja lidathanso kaamba koti...