Apezeka ndi foni m’mimba
Nthambi ya zandende m’dziko muno yaimika kaye pantchito woyang’anira ndende Emmanuel Chiganda, yemwe mkaidi amene adapezeka ndi foni ziwiri m’mimba...
Nthambi ya zandende m’dziko muno yaimika kaye pantchito woyang’anira ndende Emmanuel Chiganda, yemwe mkaidi amene adapezeka ndi foni ziwiri m’mimba...
Pomwe Amalawi lero pa 14 May akukumbukira moyo ndi utsogoleri wa mtsogoleri woyamba a Hastings Kamuzu Banda, mizwanya pa mbiri...
Komiti yoona zamalamulo m’Nyumba ya Malamulo ili mkati motolera maganizo aanthu pa zachilango chonyonga opezeka wolakwa pa milandu ya kupha,...
Kampani ya boma yogula ndi kugulitsa mbewu ya Admarc yati iyamba kugula chimanga mwezi wa mawa wa May ndipo yati...
Mtsogoleri wa Nyumba ya Malamulo a Richard Chimwendo Banda adatseka mkumano wa aphungu Lachitatu ndi langizo kwa otsutsa boma kuti...
Ali ndi zaka 17, mwanayu ankadwala matenda a muubongo omwe adabweretsanso mavuto olankhula pamoyo wake. Koma chimodzi chomwe mwanayu amakonda...
Womenyera ufulu pa nkhani zaumoyo, a George Jobe akumema makolo ndi onse omwe akusunga ana kuti aonetsetse kuti ana awo...
Akatswiri pa nkhani za ndale adandaula ndi kusasintha kwa zinthu m’dziko lino kwa zomwe zakhala zikuchitika kwa zaka zambiri. Mwa...
Nkhondo ndi anansi. Wodya naye mbale imodzi ndiye amakupereka kwa adani. Izi zapherezera kwa mwana wina wa zaka 11 yemwe...
Ndalama yatsopano ya K5 000 idayamba kugwira ntchito Lachinayi pa 24 February 2022 koma Amalawi ena akuda nayo nkhawa kuti...
Nduna ya zachuma a Sosten Gwengwe dzulo yalengeza bajeti ya 2022 mpaka 2023 yokwana K2.84 thriliyoni ndipo ati bajetiyo yapangidwa...
Lachiwiri pomwe timu ya dziko lino ya Flames inkakonzekera kukumana ndi Senegal mumpikisano wa matimu a mu Africa, mtsogoleri wa...
Chaka cha 2021 chidali chaka cha kwera nane nkwereko wakatundu, makamaka yemwe Amalawi amadalira kwambiri pamoyo wawo wa tsiku ndi...
Mfumu Katunga ya m’boma la Chikwawa yabweretsa mpungwepungwe polonga ufumu Gulupu Kaputeni pamene bwalo la milandu la High Court ku...
Komiti yoongolera zolimbana ndi mliri wa Covid-19 m’dziko muno yachenjeza kuti kachirombo koyambitsa matendawa kakufala ngati moto wolusa zomwe zachititsa...
Nyengo ya zisangalalo za Khrisimasi ndi chaka chatsopano (Nyuwere) yafika koma apolisi achenjeza kuti onse osangalala mopitiriza muyeso adzakumana ndi...
Kugula zipangizo zaulimi zotsika mtengo kuli mkati koma pofika Lachiwiri pa 7 December 2021, alimi 1 miliyoni okha, mwa alimi...
Apolisi amanga nkhwantha zitatu zachipani cha Democratic Progressive Party (DPP) powaganizira kuti anapereka malipoti abodza ku banki yokongoza maiko ndalama...
Cholinga cha mnyamatayo chidali kuyenda pansi kuchokera kwawo ku Mayani kupita ku Dedza paboma, mtunda wa makilomita 40. Iye ankalingalira...
Mabaloti achisankho chobwereza cha aphungu atatu ndi khansala mmodzi chomwe chiliko Lachiwiri likudzali afika mdziko muno dzulo (Lachisanu) ndipo bungwe...