Nkhani
-
Chomwe aimitsira mlandu wa a muluzi chidziwika lolemba
Mkulu wa bungwe loyendetsa milandu la Director of Public Prosecutions (DPP) a Masauko Chamkakala akuyembekeza kuuza Amalawi chifukwa chomwe aimitsira…
Read More » -
MEC yakonzeka kulanga osokoneza
Chisankho cha 2025 chikhoza kuzakhala umboni wa ulamuliro weniweni wa demokalase ngati bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) lizatsate malamulo…
Read More » -
Azengedwa mlandu wopha mkazi wake ku mangalande
Nyuzipepala zikuluzikulu za ku Mangalande Lachisanu zidadzala ndi nkhani ya bambo wina wa ku Malawi amene akumuganizira kuti adabaya ndi…
Read More » -
Mpungwepungwe ku msika wa fodya
Kudali mpungwepungwe kumsika wa fodya wa Kanengo mumzinda wa Lilongwe pomwe alimi adakwiya ndi mitengo ya fodya ndipo adauza ngakhale…
Read More » -
Mneneri akhala osadya komanso kumwa masiku 40
Mneneri Ellason Zande akuti anafa n’kudzukanso pomwe anasala kudya kwa masiku 40, Mulungu atawaonekera. A Zande omwe akuchita utumiki wawo…
Read More » -
Anthu 537 akusowabe chichitikileni namondwe
Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzidzi ya DoDMA yati tsopano apolisi angolengeza kuti anthu 537 omwe akusowabe chichitikireni namondwe wa…
Read More » -
Lamulo la za ngozi zadzidzidzi lanunkhira
Lamulo lounika za ngozi zogwa mwadzidzidzi latsala pang’ono kupsa malingana ndi zomwe mkulu woyang’anira zopanga malamulo ku unduna wa za…
Read More » -
Chithandizo chikhalapo?
Akadaulo osiyanasiyana ati boma likambirane ndi maiko omwe amathandiza dziko lino pa kusemphana kwawo pa nkhani yokhudza mkulu wabungwe lolimbana…
Read More » -
Athana naye Chizuma
Mkulu wa bungwe lolimbana ndi katangale ndi ziphuphu a Martha Chizuma akadali ndi ulendo wautali woteteza ntchito yawo yothana ndi…
Read More » -
Mavuto okhaokha m’ndondomeko ya AIP
Mavuto amanga nthenje m’pulogalamu ya zipangizo zaulimi zotsika mtengo ya AIP ngakhale kuti nduna ya zaulimi a Sam Kawale adalonjeza…
Read More » -
Fetereza wachinyengo wafika pamsika
Pomwe mdima pa za pulogalamu ya zipangizo zotsika mtengo ya Affordable Inputs Programme (AIP) ukubalalika, tsopano palowa nkhungu ya fetereza…
Read More » -
Kunali ku ‘night of prayer’
Mc Mooly Makuni Gondwe yemwe amagwira ntchito kundende ya dziko lino ndi mkazi wake Angela Chikho yemwe ndi msilikari anakulira…
Read More » -
Amayi oyendayenda akanizana migodi
Amayi oyendayenda sakumwera madzi chitsime chimodzi m’boma la Ntchisi polimbirana migodi. Nkhaniyi ikuti pali gulu la amayi achichepere ogulitsa matupi…
Read More » -
Wa zaka 19 apha mkazi wake wa zaka 16
Nkhanza za m’banja zikuchuluka m’dziko muno moti kalembera wa 2015 adawonetsa kuti mwa amayi 100 alionse omwe adakwatiwapo 42 adachitiridwako…
Read More » -
Aphungu akumana
Mkumano wa aphungu aku Nyumba ya Malamulo ulimkati ku Lilongwe ndipo mtsogoleri wanyumbayo a Richard Chimwendo Banda ati nkhawa zikuluzikulu…
Read More » -
Akhapana kaamba ka ufumu ku ntchisi
Anthu atatu akhapidwa mpaka kugonekedwa m’chipatala pa mkangano wa ufumu wa nyakwawa Kandanda kwa Senior Chief Kalumo m’boma la Ntchisi.…
Read More » -
Ena apeza golide pa vuto la mafuta
Pomwe Amalawi akulira ndi vuto la kusowa kwa mafuta a galimoto lomwe laimitsa ntchito zambiri makamaka zodalira mafutawo, anthu ena…
Read More » -
Chiyembekezo cha amalawi ku nyumba ya malamulo
Pomwe aphungu a ku Nyumba ya Malamulo akuyamba mkumano wawo wounika bajeti ya 2022-2023 pa 14 November 2022, Amalawi ati…
Read More » -
Kauniuni wa AIP watentha
Makomiti a Nyumba ya Malamulo omwe akuunika momwe feteleza wa AIP adagulidwira kuti ndalama zina zokwana K750 miliyoni zisokonekere aluma…
Read More » -
A chakwera sakugawa maswiti
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera achenjeza nduna zawo kuti yense osatha ntchito yake achotsedwa paudindo wake chifukwa nduna…
Read More »