Chichewa
-
Kugwiririra ana kudzatha?
Pafupufupi tsiku lililonse tikumamva kapena kuwerenga malipoti akuti mwana wagwiririridwa penapake. Omangidwa akumangidwa. Kugwira ndende ndiye kosakamba koma zikuoneka kuti…
Read More » -
Kupakula kukapitolo, JB achotsa nduna
Mtsogoleri wadziko lino Joyce Banda Lachitatu adakana kupumitsa mamulumuzana ena aboma kutsatira kupakula ndalama za boma kumene kwanyanya kulikulu la…
Read More » -
A ku Mozambique akulembetsa mavoti
Nzika zina za m’dziko la Mozambique zikulembetsa nawo m’kaundula wa mavoti ku Dedza popofuna kuti zidzavote nawo pa chisankho cha…
Read More » -
Banda adataya mwayi
Mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda adataya mwayi wosonyeza bwino lomwe kuti akudziwa chimene akuchita polimbana ndi chiwanda chidalowa kulikulu…
Read More » -
Mugwiliranji bere la mwini?
Masiku apitawa mtsikana wina adandifotokozera za momwe mphongo ina idagwirira bere lake pa msewu mumzinda wa Lilongwe. Mtsikanayu adali akungodziyendera …
Read More » -
Nam yapindulanji pa Tigresses?
Bungwe la Malawi National Council of Sports tsopano layeretsa timu ya Tigresses kuti Nam ndiyo yolakwa pankhani yoti timuyi ichotsedwe…
Read More » -
MW’s poetry off creative lane
The beginning in art is always good and promising, but once self-acclaimed artists detect gold in it and attempt to…
Read More » -
Papsa tonola, kusolola kwaphweka ku Kapitolo
Kwagwa papsa tonola kulikulu la dziko lino (Capital Hill) ku Lilongwe komwe akuluakulu ena ogwira ntchito zowerengera chuma cha boma…
Read More » -
‘Makuponi si yankho, ingosiyani’
Ngakhale boma lili kalikiliki ndi ndondomeko ya zipangizo zotsika mtengo, mphunzitsi wa zandale Joseph Chunga komanso mkulu woona zaufulu wachibadwidwe…
Read More » -
CSTU leadership risk legal action
Civil Servants Trade Union (CSTU) Mzuzu chapter has written CSTU president and CSTU national secretariat to convene a quadrennial conference…
Read More » -
Miss Malawi UK to promote tourism
Newly crowned Miss Malawi UK Alexina Phiri, who this coming weekend participates in Miss Black Africa UK, has lined up…
Read More » -
‘Chimanga cha 10kg tidyapo kangati’
Anthu ena akwiya m’dziko muno ndipo apempha boma kuti lisinthe ganizo lake lolamula bungwe la Admarc kuti lizigulitsa chimanga chosapitirira…
Read More » -
Phalombe yakonzeka kuthana ndi ngozi
Pafupifupi chaka chilichonse boma la Phalombe limakumana ndi ngozi zachilengedwe, kuthana ndi mavutowa lakhala vuto kwa zaka. Mwachitsanzo, chaka chatha…
Read More » -
Chalaka Kinnah Tom sangatole
Aganyu tidagwiritsidwa utsi titalonjezedwa ndi yemwe anali mphunzitsi wa Flames Tom Santfiet kuti Flames ikavulaza Nigeria. Nigeria idatiumbudza 2-0. Iye…
Read More » -
Kusamala ndi antchito olera ana
Ana ambiri masiku ano akuleredwa ndi antchito m’makomomu popeza makolo awo amakhala otangwanika kusaka makobidi kuntchito kapena mabizinezi. Ndipo alipo…
Read More » -
Zitukuko zothandiza Amalawi zisamafe
Patha zaka 50 kuchokera pamene dziko lino lidalandira ufulu wodzilamulira. Tikaunikira bwino momwe chuma chikuyendera m’dziko muno poyerekeza ndi momwe…
Read More » -
Ndale zosadula chitukuko zikhumudwitsa aMalawi
Kudula ntchito zimene adayambitsa atsogoleri akale a dziko lino kukuchititsa kuti Amalawi azingosaukirabe chifukwa ndalama zambiri zimangolowa m’madzi ntchitozo osamalizidwa.…
Read More » -
Wa zaka 22 akufuna uphungu
Timamva kuti achinyamata ndi atsogoleri a mawa, koma msungwana wa zaka 22 ku Nsanje wati akufuna kudzaimira chipani cha PP…
Read More » -
Escom isayerekeze kukweza magetsi—Banda
Kutsatira zomwe mkulu wa zachuma kukampani ya magetsi m’dziko muno ya Escom Delano Ulanje adauza wailesi ya MBC kuti bungweli…
Read More » -
Kanduku achotsa mfumu
Kwathina ku Mwanza pamene T/A Kanduku wachotsa gulupu Thambala komanso kulamula ena awiri kuti alipe mbuzi. Bwanamkubwa wa bomalo Gift…
Read More »