Chichewa
-
Escom, ganizirani Amalawi
Utsi sufuka popanda moto. Mwambiwu umatanthauza kuti kalikonse kamveka sikatero pachabe. Zamveka kuti bungwe la Escom likufuna kukweza magetsi, tikukhulupirira…
Read More » -
Amayi tizivulana tokhatokha?
Pali zinthu zina zoti mnzako akachita owonawe umazizwa, kuchita kakasi kuti kodi winayo waganiza bwanji? Mwachitsanzo, pali zakudya zina zoti…
Read More » -
Flames ikaluza, Tom abwerera?
Kuli nkhondo ku Calabar lero. Flames ikhala ikuphana ndi Nigeria masewero amenenso aunikire ntchito ya mphunzitsi wa Flames Tom Saintfiet.…
Read More » -
Lundu, Kaomba apita ku mwambo wa Kulamba?
Mafumu aakulu a Achewa muno m’Malawi Paramount Chief Lundu ndi Senior Chief Kaomba, akana kunena ngati apite kumwambo wa Kulamba…
Read More » -
Adzudzula JB zomanga mfumu
Mphunzitsi wa za malamulo kusukulu yaukachenjede ya Chancellor College Mwiza Nkhata wati ndi zodabwitsa kuti mtsogoleri wa dziko lino Joyce…
Read More » -
Mafumu aluzanitse mtundu
Nthawi ya mwambo wa Achewa wa Kulamba yafikanso. Paja chikhalidwe ndiye mizu ya mtundu ulionse. Achewa amasonkhana malo amodzi monga…
Read More » -
Amayi chepetsani zotsirana phalazi
Kawirikawiri nkhani ya nkhanza za m’mbanja imagonera abambo kuti ndiwo ali patsogolo kuzunza amayi. Tikaonetsetsa chiwerengero cha nkhanza za m’banja…
Read More » -
Za pasipoti ya Gaba sizikumveka
Sabatayi yakhala yomvetsa mutu ndi nkhani ya Gabadihno Mhango. Zachitika m’sabatayi aganyu zatiwawa ndipo tikufuna bungwe la FAM komanso timu…
Read More » -
Jombo ikudiliza matimu
Chalaka bakha nkhuku singatole. Linda madzi apite ndiye udziti wadala. Miyambiyi ndiyo idatsanuka m’sabatayi kaamba ka jombo yomwe idathudzula Nyerere…
Read More » -
Amalawi apindulanji ndi kutsogolera Sadc
Akuluakulu pa zachuma komanso mafumu m’dziko muno ati mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda afunika masomphenya kuti dziko lino lipindule…
Read More » -
Amalawi apindulanji?
Sabata yatha mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda adakhala wapampando wa bungwe la mgwirizano wa maiko a kumwera kwa Africa…
Read More » -
Kusiya ana akunjira muwilo
Sabata yathayi mmodzi wa awerengi a tsambali adafunsapo pankhani ya ana akunjira, makamaka mounikirapo pa zikalata zomwe makolo owabereka amasiya…
Read More » -
Chikho cha Carlsberg chafika pachimake
Thambo lagwa, chikho cha Carlsberg chaka chino chabwera ndi zake pamene anyamata ovala jombo atenga malo kugwedula matimu omwe amakula…
Read More » -
Chakwera angadze ndi kalumo kakuthwa
Mlendo ndiye adza ndi kalumo kakuthwa. Akadaulo pandale ati kusankhidwa kwa mbusa Dr Lazarus Chakwera kukhala mtsogoleri wa chipani chachikulu…
Read More » -
Aika mwala wa maziko kawiri pachipatala
Lolemba m’sabatayi mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda adatsogolera anthu a m’boma la Ntcheu pomwe amayala mwala wa maziko pa…
Read More » -
Love ya pa Zed ikutipweteka
La 40 lakwana. Zochitika ku Zambia komwe Flames imakapikisana nawo mumpikisano wa Cosafa zadziwika. Kumeneko Flames idataya bomwetamweta koma ati…
Read More » -
Tikulumirabe ana chakudya?
Masiku ano pomwe matenda a Edzi afala mwa nkhani nkhani pakufunika kuonetsetsa komanso kusintha zinthu zina zomwe anthu timachita makamaka…
Read More » -
MCP yatiphunzitsa zambiri
Nkhani idali mkamwamkamwa miyezi ingapo yapitayi ndi ya msonkhano waukulu wa chipani cha MCP. Zimakaikitsa ngati kumsonkhanowo kukamangidwe mfundo zolemekeza…
Read More » -
Apereka ambulansi ku Bangwe
Kwa kanthawi anthu makamaka amayi oyembekezera akhala akuvutika mayendedwe popita ku chipatala cha Bangwe Clinic mumzinda wa Blantyre. Anthu omwe…
Read More » -
Tom sakufunanso ndalama?
Kati deru kadazizwitsa mlenje. Ife aganyu tadzidzimuka ndi ganizo la mphunzitsi wa Flames Tom Saintfiet yemwe tsopano wanena kuti sakufunanso…
Read More »