Chichewa
-
Kaomba adandaula ndi kuchedwa kwa kalembera
Pamene gawo loyamba la ntchito yoti mbadwa za mdziko muno zikhale ndi zikalata za boma yatha, Senior Chief Kaomba ya…
Read More » -
Cama, ma Rasta asemphana pa za zionetsero
Chetechete sautsa nyama zabvumbulukadi kuti pali mangawa aakulu pakati pagulu lotsatira chikhulupiriro cha Chirasta ndi mabungwe omenyera maufulu a anthu…
Read More » -
Fetereza wa makuponi akusowa, atero ena
Pamene alimi ena ali kalikiliki kuthira fetereza wachiwiri m’minda mwawo, Tamvani yapeza kuti fetereza wa makuponi akusowa m’midzi ina ndipo…
Read More » -
Mkangano pakati pa asilamu ndi a gule
Mkokemkoke udakula ku Mitundu mumzinda wa Lilongwe Lamulungu lathali pomwe a gule wamkulu adayamba kukokanakokana ndi anthu a chipembedzo cha…
Read More » -
Cama ikuti zionetsero pa 17
Pamene nkhani yochita zionetsero pokwiya ndi utsogoleri wa Pulezidenti Joyce Banda mmene akuyendetsera dziko lino, ena mwa Amalawi otumikiridwa ati…
Read More » -
‘Khirimasi idali yovuta’
Lachiwiri lidali tsiku la Khirisimasi, ndipo anthu adali kalikiliki kugula katundu kuti asangalale ndi mabanja awo tsiku lokumbukira kubadwa kwa…
Read More » -
Imfa ya Bingu idatembenuza ndale ku Malawi
Chaka cha 2012 sichidzaiwalika m’mbiri ya dziko lino pomwe kadali koyamba kuti mtsogoleri wolamula atisiye ali pampandowu. Mtsogoleri wa dziko…
Read More » -
‘Kachali asayang’anire Bungwe la zisankho’
Bungwe lounikira za ufulu wa Amalawi komanso mgwirizano wa mabungwe pa zisankho adzudzula mtsogoleri wa dziko lino posankha wachiwiri wake…
Read More » -
JB achotsa Kachali ku EC
Mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda wabweza moto, ndipo wachotsa wachiwiri wake Khumbo Kachali pampando woyang’anira bungwe la chisankho la…
Read More » -
‘Uhule wanyanya’
Lero pa 1 Disembala ndi tsiku limene maiko onse padziko lapansi amakumbukira za nkhondo yolimbana ndi matenda a Edzi. Koma…
Read More » -
Alandira makuponi ‘abodza’ kuchoka ku boma
Mitu ya alimi ena ku Mpemba kwa T/A Somba ku Blantyre yabalalika pomwe auzidwa kuti makuponi omwe alandira ndi achinyengo.…
Read More » -
Kukweza mafumu kwalowa ndale—mafumu
Mkwezakweza wa mafumu womwe mtsogoleri wa dziko lino, Joyce Banda, wachita chitengereni mpandowu wanyanyula mafumu. Iwo apempha kuti mtsogoleriyu aziona…
Read More » -
Agwira ‘onyoza’ mtsogoleri wa dziko lino
Amayi awiri ati apolisi adawamanga sabata ikuthayi powaganizira kuti adanyoza mtsogoleri wadziko lino, Joyce Banda ndi chipani chake cha People’s…
Read More » -
Njala yafikapo, ena akugonera mango
Pali chiopsezo kuti anthu ena angafe ndi njala yomwe yagwa m’madera awo. Anthuwa ati ngakhale boma likugawa chimanga m’maboma omwe…
Read More » -
UDF ibalalika ku Nyumba ya Malamulo
Mpungwepungwe udabuka mu Nyumba ya Malamulo yomwe idatsegulidwa Lolemba pomwe aphungu a chipani cha United Democratic Front (UDF) adaonetsa kusamvana…
Read More » -
Kapito adzudzula kukweza mitengo
Patangotha sabata bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (Mera) litakweza mitengo ya magetsi ndi mafuta agalimoto, madera ena maka kumidzi…
Read More » -
Chipatala chidatha 2009, sichidatsegulidwebe
Anthu ndi mafumu ku Ligowe kwa T/A Mlauli m’boma la Neno apempha boma kuti liwatsekulire chipatala chomwe chidatha mu 2009…
Read More » -
Aimika malamulo a mathanyula
Mafumu ndi a mipingo ena adzudzula zomwe idanena nduna ya zamalamulo m’dziko muno, Ralph Kasambara kuti boma layamba laimika malamulo…
Read More » -
UDF isankha Atupele akhale tcheya
Pomwe chipani cha UDF chikusangalala kuti chachititsa msonkhano waukulu omwe ati udali wokomera anthu, katswiri pandale, Joseph Chunga komanso mulumuzana…
Read More » -
Aziputa dala
Amuna ambiri amakonda zongotenga asungwana osawadziwa n’kukagona nawo ku maresitihausi. Zikatha bwino, amaoneka wochenjera. Komatu amaiwala kuti nthawi zina akhoza…
Read More »