Monday, May 16, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

‘Takulira limodzi, kuchokera ubwana’

by Martha Chirambo
20/02/2022
in Chichewa
2 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

 Lucius Banda adaimba nyimbo yomwe imati: Takulira limodzi, kuyambira ubwana…. Kusiyana kwake n’koti anthu amaimbidwa m’nyimboyo mapeto sadakwatirane. Si zili choncho ndi achikondi awiri amene zonse zidakathera m’banja.

Geoffrey Chanza ndi Getrude Ghambi adakumana ali achichepere. Iwowa akula limodzi ku Engucwini m’boma la Mzimba komwenso amapemphera mpingo umodzi.

Panthawiyi awiriwo akuti amangodziwana ngati anthu basi koma panalibe chilichonse pakati pawo komanso samachezerana.

Koma zinthu zinasintha 2016 Getrude akuchita maphunziro ake a unamwino m’chaka choyamba.

Geoffrey and Getrude tsiku la ukwati wawo

“Tidakumana patsamba la m’chezo la Facebook n’kuyamba kucheza. Tinapatsana manambala n’kumacheza pa Whatsapp,” adatero iye.

Malinga ndi Gertrude awiriwo adakumananso ku Mzuzu panthawi ya tchuthi.

“Geoffrey anandiuza mawu kuti wakhala akundifuna koma amaopa kundiuza. Ndinamuyankha kuti andipatse nthawi chifukwa ine ndinkamutenga ngati mnzanga ndipo sindinkachimva mkati mwanga,” anatero Getrude.

Koma pofika 2018, chibwenzi cha awiriwo chinayamba.

“Patadutsa miyezi yochepa, tinadzasiyananso chifukwa cha nkhani zina ndi zina. Koma patadutsa miyezi itatu tinabwererana,” anatero Getrude.

Awiriwo anakhala zaka zitatu pa ubwenzi. Ndipo pa December 11, 2021 anadalitsa ukwati wawo pa St Augustine Catholic mumzinda wa Mzuzu.

Iwo akulangiza anthu omwe akufuna banja kuti adekhe ndi kudikira pa Mulungu.

Iwo adatinso mavuto omwe amakumana nawo ambiri amathana nawo powapereka m’manja mwa Mulungu.

Getrude ndi namwino komanso mzamba pachipatala cha boma ku Nkhata Bay pomwe Geoffrey amagwira ntchito ku Vision Fund.

Awiriwo akukhala m’boma la Nkhata Ba

Previous Post

Zaluso Arts in $50 000 Zalero project

Next Post

Tigresses crowned Rainbow champions

Related Posts

Foni kundende monga ya Zomba n’zoletsedwa
Nkhani

Apezeka ndi foni m’mimba

May 15, 2022
A Kamuzu adali katakwe pandale
Nkhani

‘Kamuzu adali chitsime chakuya’

May 14, 2022
Kodi chilango chonyonga chikhalepo, kapena ayi?
Nkhani

Amalawi akupereka maganizo pa zonyonga

May 14, 2022
Next Post

Tigresses crowned Rainbow champions

Opinions and Columns

Candid Talk

Know your place in his/her life

May 15, 2022
People’s Tribunal

Why can’t we start with implementing the reforms?

May 15, 2022
Big Man Wamkulu

My wife is a WhatsApp addict

May 15, 2022
My Thought

Two years of nothing but development rallies

May 15, 2022

Trending Stories

  • Chakaka-Nyirenda: The DPP will look into it

    Embassy assets sold, money untraceable

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • PAC clears Macra director general, cautions board

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Tonse cracks suspicions grow

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Two years of nothing but development rallies

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • My wife is a WhatsApp addict

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.