Tuesday, June 28, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

‘Tinkakalongosola za ntchito’

by Steven Pembamoyo
22/11/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

 

Okaona nyanja amakawonadi ndi mvuu zomwe. Mawuwa apherezedwa ndi ukwati wa Amos Mazinga wa ku Dowa m’mudzi mwa Ngozi T/A Chiwere ndi Regina Mkonda wa ku Mulanje mmudzi mwa Reuben.

Awiriwa akuti adakumana kuofesi ya maphunziro ku Nathenje mu 2014 atamaliza maphunziro a zauphunzitsi komwe amakolongosola za komwe azikagwirira ntchito.

Amos adati iye atangomuona Regina, mtima wake udadumpha kwambiri.

Amos ndi Rehina kupsopsonana tsiku la ukwati wawo
Amos ndi Rehina kupsopsonana tsiku la ukwati wawo

“Ndine mmodzi mwa anthu omasuka ngakhale pagulu koma tsikulo ndidaona nyenyezi yothobwa mmaso,” adatero Amos.

Iye akuti panthawi yomwe iwo amayembekezera kuthandizidwa, mpamene adapeza mwayi wolankhulana ndi msungwanayo ndipo adacheza bwino mpaka kupatsana nambala za foni.

Kusiyana kwa pamenepo kudali madzulo atalandira thandizo koma kudali kusiyana pamaso chabe chifukwa macheza awo adapitirira kudzera palamya.

“Tidakhala nthawi yaitali tikuchezerana palamya mpaka tsiku lina nditalimba mtima ndidayambitsa nkhani ya chikondi koma kunena zoona ndidalimbana naye mpaka adatheka,” adatero Amos.

Iye akuti chikondi chake pa Regina chidakula kwambiri kaamba ka khalidwe lake lokonda kupemphera, kuchita zinthu mwa nzeru ndi modzilemekeza komanso mwasangala.

Regina adati iye poyamba adamutenga Amos ngati mchimwene koma pang’onopang’ono chikondi chidayamba kumugwira moti samafunanso kuti Amos adzagwe m’manja mwa munthu wina koma iye.

Iye adati ngakhale amakanakana poyamba, mtima wake udali utalola kale koma amafuna kuona ngati Amos adalidi munthu wachilungamo wosangofuna kumuseweretsa.

“Sindidafune munthu woti kugwa naye m’chikondi panthawi yochepa kenako nkukhumudwitsidwa ndiye ndimayenera kuonetsetsa kuti ndikudzipereka m’manja oyeneradi,” adatero Regina.

Ukwati adamangitsa kumpingo wa CCAP.

 

Previous Post

Who is evangelist Shadreck Wame?

Next Post

Constructing a basic hand washing facility

Related Posts

Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Katundu wa a Mtambo adali kuseri kwa ofesi za khonsolo
Nkhani

Agona ku maofesi a khonsolo ya Mzuzu

June 4, 2022
Nkhani

Woimba abedwa mumzinda wa mzuzu

May 28, 2022
Next Post

Constructing a basic hand washing facility

Opinions and Columns

People’s Tribunal

Two years later and we are still singing same song

June 26, 2022
Big Man Wamkulu

Wife’s relatives have taken over my house

June 26, 2022
My Thought

Stop cyber harassment

June 26, 2022
Candid Talk

Baby gender preference and disappointments

June 26, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • Changaya: It is a
huge trade deal

    K243bn Malawi trade deal on rocks

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • ACB cleared Sattar contract—Documents

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Britain squeezes Zuneth Sattar

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Wife’s relatives have taken over my house

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Police arrest Treasury official for alleged fraud

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.