Wednesday, May 18, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Adverts
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Tomato wabooka pa Bembeke

by Bobby Kabango
09/05/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Alimi ku Bembeke m’boma la Dedza ayamba kufupa tomato wawo pamene wachoka pa mtengo wa K6 000 pa dengu kufika pa K1 000.
Izi zikuchitika chifukwa cha kuchuluka kwa tomato amene akufika pamsikawu zomwe zachititsa kuti anthu opita ku Lilongwe kapena ku Blantyre azigula tomatoyu.

Kutapa kutaya: Tomato amafunika kusamala
Kutapa kutaya: Tomato amafunika kusamala

Malinga ndi mmodzi mwa alimiwa, Akisa Magugu, mwezi wa March amagulitsa dengu pa mtengo wa K6 000 koma pano watsikiratu.
“Tikungofupa tomato, taganizani dengu lomwe timagulitsa K6 000 miyezi yangothayi lero latsika ndipo likupita pa mtengo wa K1 000 ndipo zikavuta akumagula pa mtengo wa K500.
“Taononga ndalama zambiri kuti tomatoyu tilime koma mapeto ake tangoyamba kufunano kwa anthu mopweteka kwambiri chifukwa tomato amene mumamuona pamsikawu sachoka pafupi,” adatero Magugu.
Kulira kwa Magugu mwina kungathe ndi ganizo lomwe mkonzi wa pulogalamu ya Ulimi wa Lero Excello Zidana, yemwe ndi mlangizi wa zaulimi, akunena: “Vuto ndi alimiwa chifukwa amayamba kulima asadapeze msika. Ndi bwino alimi asadalime adziyamba aona msika momwe ulili komanso kumatchera nyengo yake chifukwa zimathandiza kuti idziwe nthawi yomwe mbewuyo imagulika bwino.”
Zidana akuti ndi bwinonso alimiwa aziyang’ana msika wina ngati zinthu zavuta choncho. “Kuti upite madera ena upeza alimi akupha makwacha ndi mbewu yomweyo. Ayende misika ina ndithu akasimba mwayi,” adatero.

Tags: tomatoulimi m'malawi
Previous Post

Ulangizi wa pafoni uthandiza alimi

Next Post

Bwalo La Ulimi: Ma trawler aunikidwe

Related Posts

Foni kundende monga ya Zomba n’zoletsedwa
Nkhani

Apezeka ndi foni m’mimba

May 15, 2022
A Kamuzu adali katakwe pandale
Nkhani

‘Kamuzu adali chitsime chakuya’

May 14, 2022
Kodi chilango chonyonga chikhalepo, kapena ayi?
Nkhani

Amalawi akupereka maganizo pa zonyonga

May 14, 2022
Next Post

Bwalo La Ulimi: Ma trawler aunikidwe

Opinions and Columns

Candid Talk

Know your place in his/her life

May 15, 2022
People’s Tribunal

Why can’t we start with implementing the reforms?

May 15, 2022
Big Man Wamkulu

My wife is a WhatsApp addict

May 15, 2022
My Thought

Two years of nothing but development rallies

May 15, 2022

Trending Stories

  • A fleet of UTM vehicles: The movement says it is funded by well-wishers

    UTM party vehicle issue goes to MRA

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • What bloody chieftaincy!

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • PAC clears Macra director general, cautions board

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Firm discovers copper deposits

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Investment pledges jump to K666 billion

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

Malawi-Music.com Top10

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.